A-Z Lyrics Database
Welcome! Login | Register
Lyrics   »   C   »   Chifundo Chikonga Lyrics   »   Amayankha Lyrics

Chifundo Chikonga - Amayankha Lyrics

Font:      
Align:    
  • Ho-yee mama wee! ah yeah
  • Ooh yeah aah mthefile
  • O! mama wee!
  • Anali kuti dzana, mtima utawawa
  • Nkhawa zitafika, anabwerera m'mbuyo
  • Analira kosatha, usiku ndi usana
  • Atasweka mtima m'vuto lawo
  • Anamuuza Yesu, atathedwa nzeru
  • Anayembekeza, amayankha
  • Anamuuza Yesu, atathedwa nzeru
  • Anayembekeza, amayankha
  • Chorus
  • Anamuuza Yesu (Amayankha)
  • Anayitanirabe (Amayankha)
  • Dzina la Yehova (Amayamkha)
  • Zonse zinasintha (Amayankha)
  • Amayankha... yeah ihh
  • Anali kuti dzana, litavuta banja
  • Atakhumudwitsidwa misonzi ikutsika
  • Anadera nkhawa ntchito itasowa
  • Anavomereza kuti sadzayipeza
  • Anamuuza Yesu, atathedwa nzeru
  • Anayembekeza poti amayankha
  • Anamuuza Yesu, atathedwa nzeru
  • Anayembekeza ena nkumadabwa
  • Chorus
  • Anamuuza Yesu (Amayankha)
  • Anayitanirabe (Amayankha)
  • Dzina la Yehova (Amayamkha)
  • Zonse zinasintha (Amayankha)
  • Amayankha ah oh Amayankha
  • Bridge
  • Nanga ukulira chani iwe?
  • Pukuta misonzi
  • Zabwino zidzera oh, iwo oyembekeza, ooh uohuh!
  • Chorus til end

  • Report error in lyric




    Latest Chifundo Chikonga Lyrics

    The Amayankha lyrics by Chifundo Chikonga is property of their respective authors, artists and labels and are strictly for non-commercial use only.
    Copyright © 2009-2026 Azlyricdb.com. All Rights Reserved | Privacy policy | Blog
    You are now viewing Chifundo Chikonga Amayankha Lyrics